1 Inu Aisraeli, imvani mawu awa amene Yehova wayankhula kutsutsana nanu, kutsutsana ndi banja lonse limene analitulutsa mu Igupto:
2 “Inu nokha ndi amene ndinakusankhani
3 Kodi anthu awiri nʼkuyendera limodzi
4 Kodi mkango umabangula mʼnkhalango
5 Kodi mbalame nʼkutera pa msampha
6 Kodi pamene lipenga la nkhondo lalira mu mzinda,
7 Zoonadi Ambuye Yehova sachita kanthu
8 Mkango wabangula,
9 Lengezani zimenezi ku nyumba zaufumu za ku Asidodi
10 “Iwo sadziwa kuchita zolungama,
11 Nʼchifukwa chake Ambuye Yehova akunena izi:
12 Yehova akuti,
13 “Imvani izi ndipo mupereke umboni wotsutsa nyumba ya Yakobo,” akutero Ambuye, Yehova Mulungu Wamphamvuzonse.
14 “Pa tsiku limene ndidzalange Israeli chifukwa cha machimo ake,
15 Ndidzagwetsa nyumba ya pa nthawi yozizira