1 Yehova akuti,
2 Ine ndidzatumiza moto pa Mowabu,
3 Ndidzawononga wolamulira wake
4 Yehova akuti,
5 Ine ndidzatumiza moto pa Yuda,
6 Yehova akuti,
7 Amapondereza anthu osauka
8 Anthuwo amakagonana mʼmbali mwa guwa lililonse la nsembe
9 “Ine ndinawononga Aamori pamaso pawo,
10 “Ine ndinakutulutsani ku Igupto,
11 Ine ndinawutsanso ena mwa ana ako kuti akhale aneneri,
12 “Koma inu munawamwetsa vinyo anaziri aja,
13 “Tsono Ine ndidzakupsinjani
14 Munthu waliwiro sadzatha kuthawa,
15 Munthu wa uta sadzalimbika,
16 Ngakhale asilikali olimba mtima kwambiri