1 Mawu a Amosi, mmodzi mwa anthu oweta nkhosa ku Tekowa. Zimene iye anaona mʼmasomphenya zokhudza Israeli patatsala zaka ziwiri kuti chivomerezi chichitike, nthawi imene Uziya anali mfumu ya Yuda ndipo Yeroboamu mwana wa Yowasi anali mfumu ya Israeli.
2 Amosi anati:
3 Yehova akuti,
4 Ine ndidzatumiza moto pa nyumba ya Hazaeli
5 Ndidzathyola chipata cha Damasiko;
6 Yehova akuti,
7 ndidzatumiza moto pa makoma a Gaza
8 Ndidzawononga mfumu ya ku Asidodi
9 Yehova akuti,
10 Ine ndidzatumiza moto pa makoma a Turo
11 Yehova akuti,
12 Ine ndidzatumiza moto pa Temani
13 Yehova akuti,
14 Ine ndidzayatsa moto pa makoma a ku Raba
15 Mfumu yawo idzatengedwa kupita ku ukapolo,