1 Crônicas 2

NYA

1 Ana a Israeli anali awa:

2 Dani, Yosefe, Benjamini, Nafutali, Gadi ndi Aseri.

3 Ana a Yuda anali awa:

4 Mpongozi wake Tamara anamuberekera Perezi ndi Zera. Ana onse a Yuda analipo asanu.

5 Ana a Perezi anali awa:

6 Ana a Zera anali awa:

7 Mwana wa Karimi anali

8 Mwana wa Etani anali

9 Ana amene anabadwa kwa Hezironi anali:

10 Ramu anabereka

11 Naasoni anabereka Salima, Salima anabereka Bowazi,

12 Bowazi anabereka Obedi ndipo Obedi anabereka Yese.

13 Yese anabereka

14 wachinayi Netaneli, wachisanu Radai,

15 wachisanu ndi chimodzi Ozemu ndi wachisanu ndi chiwiri Davide.

16 Alongo awo anali Zeruya ndi Abigayeli. Ana atatu a Zeruya anali Abisai Yowabu ndi Asaheli.

17 Abigayeli anali amayi ake a Amasa amene abambo ake anali Yeteri wa fuko la Ismaeli.

18 Kalebe mwana wa Hezironi anabereka ana mwa Azuba mkazi wake (ndi mwa Yerioti). Ana a mkaziyo anali awa: Yeseri, Sobabu ndi Aridoni.

19 Azuba atamwalira, Kalebe anakwatira Efurata, amene anamuberekera Huri.

20 Huri anabereka Uri ndipo Uri anabereka Bezaleli.

21 Patapita nthawi, Hezironi anagona ndi mwana wamkazi wa Makiri abambo ake a Giliyadi (iye anamukwatira ali ndi zaka 60) ndipo anamuberekera Segubu.

22 Segubu anabereka Yairi, amene anali ndi mizinda 23 ku Giliyadi.

23 (Koma Gesuri ndi Aramu analanda Havoti Yairi komanso Kenati ndi madera ake onse ozungulira, mizinda makumi asanu ndi umodzi). Onsewa anali adzukulu, a Makiri abambo ake a Giliyadi.

24 Atamwalira Hezironi ku Kalebe Efurata, Abiya mkazi wa Hezironi anamuberekera Asihuri abambo a Tekowa.

25 Ana a Yerahimeeli, mwana woyamba wa Hezironi anali:

26 Yerahimeeli anali ndi mkazi wina amene dzina lake linali Atara, amene anali amayi a Onamu.

27 Ana a Ramu, mwana woyamba wa Yerahimeeli, anali awa:

28 Ana a Onamu anali awa:

29 Mkazi wa Abisuri anali Abihaili, amene anamuberekera Ahibani ndi Molidi.

30 Ana a Nadabu anali awa:

31 Ana a Apaimu anali awa:

32 Ana a Yada, mʼbale wa Samai, anali awa:

33 Ana a Yonatani anali awa:

34 Sesani sanabereke ana aamuna koma aakazi okhaokha.

35 Sesani anapereka mwana wake wamkazi kwa Yariha wantchito wake kuti amukwatire ndipo anamuberekera Atayi.

36 Atayi anali abambo ake a Natani,

37 Zabadi anali abambo a Efilali,

38 Obedi anali abambo a Yehu,

39 Azariya anali abambo a Helezi,

40 Eleasa anali abambo ake a Sisimai,

41 Salumu anali abambo a Yekamiya,

42 Ana a Kalebe mʼbale wa Yerahimeeli anali awa:

43 Ana a Hebroni anali awa:

44 Sema anali abambo ake Rahamu ndipo Rahamu anali abambo a Yorikeamu. Rekemu anali abambo a Samai.

45 Mwana wa Samai anali Maoni, ndipo Maoni anali abambo a Beti Zuri.

46 Efai, mzikazi wa Kalebe, anali amayi a Harani, Moza ndi Gazezi. Harani anali abambo a Gazezi.

47 Ana a Yahidai anali awa:

48 Maaka mzikazi wa Kalebe anali mayi Seberi ndi Tirihana.

49 Iye anaberekanso Saafi abambo a Madimena ndi Seva abambo a Makibena ndi Gibeya. Mwana wamkazi wa Kalebe anali Akisa.

50 Izi zinali zidzukulu za Kalebe.

51 Salima abambo a Betelehemu ndi Harefu abambo ake a Beti-Gadera.

52 Zidzukulu za Sobala abambo a Kiriati Yearimu zinali izi:

53 ndipo mabanja a Kiriati-Yeyarimu anali awa: Aitiri, Aputi, Asumati ndi Amisirai. Azorati ndi Aesitaoli anachokera kwa amenewa.

54 Zidzukulu za Salima zinali izi:

55 ndiponso mabanja a alembi amene amakhala ku Yabesi: Atiroti, Asimeati ndiponso Asukati. Awa ndi Akeni amene anachokera kwa Hamati, kholo la Arekabu.

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado