1 Crônicas 3

NYA

1 Ana aamuna a Davide amene anabadwira ku Hebroni anali awa:

2 wachitatu anali Abisalomu, mwana wa Maaka mwana wa Talimai mfumu ya Gesuri;

3 wachisanu anali Sefatiya, amayi ake anali Abitali;

4 Ana asanu ndi mmodzi awa a Davide anabadwira ku Hebroni kumene analamulirako zaka zisanu ndi ziwiri ndi miyezi isanu ndi umodzi.

5 ndipo ana amene anabadwira ku Yerusalemuko anali awa:

6 Anaberekanso Ibihari, Elisua, Elipeleti,

7 Noga, Nefegi, Yafiya,

8 Elisama, Eliada ndi Elifeleti, onse analipo asanu ndi anayi.

9 Onsewa anali ana a Davide, osawerengera ana a azikazi. Ndipo mlongo wawo anali Tamara.

10 Mwana wa Solomoni anali Rehabiamu,

11 Yehosafati anabereka Yehoramu,

12 Yowasi anabereka Amaziya,

13 Yotamu anabereka Ahazi,

14 Manase anabereka Amoni,

15 Ana a Yosiya anali awa:

16 Ana a Yehoyakimu:

17 Zidzukulu za Yekoniya wa mʼndende zinali izi:

18 Malikiramu, Pedaya, Senazara, Yekamiya, Hosama ndi Nedabiya.

19 Ana a Pedaya anali awa:

20 Panalinso ana ena asanu awa:

21 Zidzukulu za Hananiya zinali izi:

22 Zidzukulu za Sekaniya zinali izi:

23 Ana a Neariya anali awa:

24 Ana a Eliyoenai: Hodaviya, Eliyasibu, Pelaya, Akubu,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado