1 Ana aamuna a Davide amene anabadwira ku Hebroni anali awa:
2 wachitatu anali Abisalomu, mwana wa Maaka mwana wa Talimai mfumu ya Gesuri;
3 wachisanu anali Sefatiya, amayi ake anali Abitali;
4 Ana asanu ndi mmodzi awa a Davide anabadwira ku Hebroni kumene analamulirako zaka zisanu ndi ziwiri ndi miyezi isanu ndi umodzi.
5 ndipo ana amene anabadwira ku Yerusalemuko anali awa:
6 Anaberekanso Ibihari, Elisua, Elipeleti,
7 Noga, Nefegi, Yafiya,
8 Elisama, Eliada ndi Elifeleti, onse analipo asanu ndi anayi.
9 Onsewa anali ana a Davide, osawerengera ana a azikazi. Ndipo mlongo wawo anali Tamara.
10 Mwana wa Solomoni anali Rehabiamu,
11 Yehosafati anabereka Yehoramu,
12 Yowasi anabereka Amaziya,
13 Yotamu anabereka Ahazi,
14 Manase anabereka Amoni,
15 Ana a Yosiya anali awa:
16 Ana a Yehoyakimu:
17 Zidzukulu za Yekoniya wa mʼndende zinali izi:
18 Malikiramu, Pedaya, Senazara, Yekamiya, Hosama ndi Nedabiya.
19 Ana a Pedaya anali awa:
20 Panalinso ana ena asanu awa:
21 Zidzukulu za Hananiya zinali izi:
22 Zidzukulu za Sekaniya zinali izi:
23 Ana a Neariya anali awa:
24 Ana a Eliyoenai: Hodaviya, Eliyasibu, Pelaya, Akubu,