1 Crônicas 1

NYA

1 Adamu, Seti, Enosi

2 Kenani, Mahalaleli, Yaredi,

3 Enoki, Metusela, Lameki, Nowa.

4 Ana a Nowa,

5 Ana aamuna a Yafeti anali:

6 Ana aamuna a Gomeri anali:

7 Ana aamuna a Yavani anali:

8 Ana aamuna a Hamu anali:

9 Ana aamuna a Kusi anali:

10 Kusi anali abambo a Nimurodi amene anali wankhondo wamphamvu

11 Igupto ndiye kholo la

12 Apaturusi, Akasilu (kumene kunachokera Afilisti) ndi Akafitori.

13 Kanaani anabereka mwana wake wachisamba Sidoni,

14 Ayebusi, Aamori, Agirigasi

15 Ahivi, Aariki, Asini

16 Aaravadi, Azemari ndi Ahamati.

17 Ana aamuna a Semu anali:

18 Aripakisadi anabereka Sela

19 Eberi anabereka ana aamuna awiri:

20 Yokitani anabereka

21 Hadoramu, Uzali, Dikila

22 Obali, Abimaeli, Seba,

23 Ofiri, Havila ndi Yobabu. Onsewa anali ana aamuna a Yokitani.

24 Semu, Aripakisadi, Sela

25 Eberi, Pelegi, Reu

26 Serugi, Nahori, Tera

27 ndi Abramu (amene ndi Abrahamu).

28 Ana a Abrahamu ndi awa:

29 Zidzukulu zake zinali izi:

30 Misima, Duma, Masa, Hadadi, Tema,

31 Yeturi, Nafisi ndi Kedema. Awa anali ana a Ismaeli.

32 Ana a Ketura mzikazi wa Abrahamu anali awa:

33 Ana aamuna a Midiyani anali,

34 Abrahamu anabereka Isake.

35 Ana aamuna a Esau anali awa:

36 Ana a Elifazi anali awa:

37 Ana a Reueli anali awa:

38 Ana a Seiri anali awa:

39 Ana aamuna a Lotani anali awa:

40 Ana aamuna a Sobala anali awa:

41 Mwana wa Ana anali

42 Ana aamuna a Ezeri anali awa:

43 Awa ndi mafumu amene ankalamulira dziko la Edomu, mfumu iliyonse ya Israeli isanayambe kulamulira kumeneko:

44 Bela atamwalira, Yobabu mwana wa Zera wochokera ku Bozira analowa ufumu mʼmalo mwake.

45 Yobabu atamwalira, Husamu wochokera ku dziko la Atemani, analowa ufumu mʼmalo mwake.

46 Husamu atamwalira, Hadadi mwana wa Bedadi, amene anagonjetsa Amidiyani mʼdziko la Mowabu, analowa ufumu mʼmalo mwake. Mzinda wake unkatchedwa Aviti.

47 Hadadi atamwalira, Samila wochokera ku Masireka analowa ufumu mʼmalo mwake.

48 Samila atamwalira, Sauli wochokera ku Rehoboti wa ku Mtsinje analowa ufumu mʼmalo mwake.

49 Sauli atamwalira, Baala-Hanani mwana wa Akibori analowa ufumu mʼmalo mwake.

50 Pamene Baala-Hanani anamwalira, Hadadi analowa ufumu mʼmalo mwake. Mzinda wake unkatchedwa Pau, ndipo dzina la mkazi wake linali Mehatabeli mwana wa Matiredi, mwana wamkazi wa Me-Zahabu.

51 Hadadi anamwaliranso.

52 Oholibama, Ela, Pinoni,

53 Kenazi, Temani, Mibezari,

54 Magidieli ndi Iramu. Awa anali mafumu a ku Edomu.

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado