Zacarias 9

NYA

1 Mawu a Yehova odzudzula dziko la Hadiraki

2 ndiponso mzinda wa Hamati, umene ukuchita malire ndi dzikoli,

3 Ndipo Turo anadzimangira linga;

4 Taonani Ambuye adzamulanda chuma chakecho

5 Mzinda wa Asikeloni udzaona zimenezi, nʼkuchita mantha;

6 Mu Asidodi mudzakhala mlendo,

7 Ndidzachotsa nyama ya magazi mʼkamwa mwawo,

8 Koma Ine ndidzalondera Nyumba yanga

9 Sangalala kwambiri, iwe mwana wamkazi wa Ziyoni!

10 Ndidzachotsa magaleta ankhondo ku Efereimu

11 Tsono kunena za iwe, chifukwa cha magazi a pangano lako ndi Ine,

12 Bwererani ku malo anu otetezedwa, inu amʼndende achiyembekezo;

13 Ndidzakoka Yuda monga ndimakokera uta wanga,

14 Pamenepo Yehova adzaonekera kwa anthu ake;

15 ndipo Yehova Wamphamvuzonse adzawateteza.

16 Tsiku limenelo Yehova Mulungu wawo adzawapulumutsa

17 Taonani chikoka ndi kukongola kwawo!

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado