1 Mawu a Yehova odzudzula dziko la Hadiraki
2 ndiponso mzinda wa Hamati, umene ukuchita malire ndi dzikoli,
3 Ndipo Turo anadzimangira linga;
4 Taonani Ambuye adzamulanda chuma chakecho
5 Mzinda wa Asikeloni udzaona zimenezi, nʼkuchita mantha;
6 Mu Asidodi mudzakhala mlendo,
7 Ndidzachotsa nyama ya magazi mʼkamwa mwawo,
8 Koma Ine ndidzalondera Nyumba yanga
9 Sangalala kwambiri, iwe mwana wamkazi wa Ziyoni!
10 Ndidzachotsa magaleta ankhondo ku Efereimu
11 Tsono kunena za iwe, chifukwa cha magazi a pangano lako ndi Ine,
12 Bwererani ku malo anu otetezedwa, inu amʼndende achiyembekezo;
13 Ndidzakoka Yuda monga ndimakokera uta wanga,
14 Pamenepo Yehova adzaonekera kwa anthu ake;
15 ndipo Yehova Wamphamvuzonse adzawateteza.
16 Tsiku limenelo Yehova Mulungu wawo adzawapulumutsa
17 Taonani chikoka ndi kukongola kwawo!