1 Pemphani mvula kwa Yehova pa nthawi yamphukira;
2 Mafano amayankhula zachinyengo,
3 “Ine ndawakwiyira kwambiri abusa,
4 Mu Yuda mudzachokera mwala wapangodya,
5 Onse pamodzi adzakhala ngati ngwazi zankhondo
6 “Ndidzalimbitsa nyumba ya Yuda
7 Aefereimu adzakhala ngati ankhondo amphamvu
8 Ndidzaliza mluzu
9 Ndinawamwaza pakati pa mitundu ina ya anthu,
10 Ndidzawabweretsa kuchokera ku Igupto
11 Adzawoloka nyanja ya masautso;
12 Ndidzalimbitsa iwo mwa Yehova