1 “Andizunza kwambiri kuyambira ubwana wanga,”
2 “Andizunza kwambiri kuyambira ubwana wanga,
3 Anthu otipula analima pa msana panga
4 Koma Yehova ndi wolungama;
5 Onse amene amadana ndi Ziyoni
6 Akhale ngati udzu womera pa denga la nyumba,
7 sungadzaze manja a owumweta
8 Odutsa pafupi asanene kuti,