Salmos 128

NYA

1 Odala ndi onse amene amaopa Yehova,

2 Udzadya chipatso cha ntchito yako;

3 Mkazi wako adzakhala ngati mpesa wobereka

4 Ameneyu ndiye munthu wodalitsidwa

5 Yehova akudalitse kuchokera mʼZiyoni

6 ndipo ukhale ndi moyo kuti udzaone zidzukulu zako.

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado