Salmos 118

NYA

1 Yamikani Yehova chifukwa ndi wabwino;

2 Israeli anene kuti:

3 Banja la Aaroni linene kuti,

4 Iwo amene amaopa Yehova anene kuti:

5 Ndili mʼmasautso anga ndinalirira Yehova,

6 Yehova ali nane; sindidzachita mantha.

7 Yehova ali nane; Iye ndiye thandizo langa.

8 Nʼkwabwino kuthawira kwa Yehova

9 Nʼkwabwino kuthawira kwa Yehova

10 Anthu a mitundu yonse anandizinga,

11 Anandizinga mbali zonse,

12 Anandizinga ngati njuchi,

13 Anandikankha uku ndi uko ndipo ndinali pafupi kugwa,

14 Yehova ndiye mphamvu yanga ndi nyimbo yanga;

15 Mfuwu wachimwemwe ndi chipambano

16 Dzanja lamanja la Yehova latukulidwa mmwamba

17 Sindidzafa koma ndidzakhala ndi moyo

18 Yehova wandilanga koopsa,

19 Tsekulireni zipata zachilungamo,

20 Ichi ndicho chipata cha Yehova

21 Ndidzakuyamikani chifukwa Inu munandiyankha;

22 Mwala umene amisiri omanga nyumba anawukana

23 Yehova ndiye wachita zimenezi

24 Lero ndiye tsiku limene Yehova walipanga;

25 Inu Yehova, tipulumutseni;

26 Wodala amene akubwera mʼdzina la Yehova.

27 Yehova ndi Mulungu,

28 Inu ndinu Mulungu wanga, ndipo ndidzakuyamikani;

29 Yamikani Yehova chifukwa ndi wabwino;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado