1 Yamikani Yehova chifukwa ndi wabwino;
2 Israeli anene kuti:
3 Banja la Aaroni linene kuti,
4 Iwo amene amaopa Yehova anene kuti:
5 Ndili mʼmasautso anga ndinalirira Yehova,
6 Yehova ali nane; sindidzachita mantha.
7 Yehova ali nane; Iye ndiye thandizo langa.
8 Nʼkwabwino kuthawira kwa Yehova
9 Nʼkwabwino kuthawira kwa Yehova
10 Anthu a mitundu yonse anandizinga,
11 Anandizinga mbali zonse,
12 Anandizinga ngati njuchi,
13 Anandikankha uku ndi uko ndipo ndinali pafupi kugwa,
14 Yehova ndiye mphamvu yanga ndi nyimbo yanga;
15 Mfuwu wachimwemwe ndi chipambano
16 Dzanja lamanja la Yehova latukulidwa mmwamba
17 Sindidzafa koma ndidzakhala ndi moyo
18 Yehova wandilanga koopsa,
19 Tsekulireni zipata zachilungamo,
20 Ichi ndicho chipata cha Yehova
21 Ndidzakuyamikani chifukwa Inu munandiyankha;
22 Mwala umene amisiri omanga nyumba anawukana
23 Yehova ndiye wachita zimenezi
24 Lero ndiye tsiku limene Yehova walipanga;
25 Inu Yehova, tipulumutseni;
26 Wodala amene akubwera mʼdzina la Yehova.
27 Yehova ndi Mulungu,
28 Inu ndinu Mulungu wanga, ndipo ndidzakuyamikani;
29 Yamikani Yehova chifukwa ndi wabwino;