1 Miyambo ya Solomoni:
2 Chuma chochipeza mwachinyengo sichipindulitsa,
3 Yehova salola kuti munthu wolungama azikhala ndi njala;
4 Wochita zinthu mwaulesi amasauka,
5 Amene amakolola nthawi yachilimwe ndi mwana wanzeru,
6 Madalitso amakhala pa mutu wa munthu wolungama,
7 Munthu wolungama anzake adzamukumbukira ngati mdalitso,
8 Munthu wa mtima wanzeru amasamala malamulo,
9 Munthu woyenda mwangwiro amayenda mosatekeseka;
10 Aliyense wotsinzinira maso mwachinyengo amabweretsa mavuto,
11 Pakamwa pa munthu wolungama ndi kasupe wamoyo,
12 Udani umawutsa mikangano,
13 Nzeru imapezeka pa milomo ya munthu wozindikira zinthu,
14 Anzeru amasunga chidziwitso
15 Chuma cha munthu wolemera
16 Moyo ndiye malipiro a munthu wolungama,
17 Wosamalira malangizo amayenda mʼnjira ya moyo,
18 Amene amabisa chidani chake ndi munthu wonama,
19 Mawu akachuluka zolakwa sizisowa,
20 Mawu a munthu wolungama ali ngati siliva wabwino kwambiri,
21 Milomo ya anthu olungama imalimbikitsa ambiri;
22 Mdalitso wa Yehova ndiwo umabweretsa chuma,
23 Kwa chitsiru kuchita zinthu zoyipa ndiye chinthu chomusangalatsa,
24 Chimene munthu woyipa amachiopa chidzamuchitikira;
25 Pamene namondwe wawomba, anthu oyipa amachotsedwa,
26 Momwe amakhalira vinyo wosasa mʼkamwa ndi momwe umakhalira utsi mʼmaso,
27 Kuopa Yehova kumatalikitsa moyo;
28 Chiyembekezo cha olungama chimapatsa chimwemwe,
29 Njira za Yehova ndi linga loteteza anthu ochita zabwino,
30 Munthu wolungama sadzachotsedwa, pamalo pake
31 Pakamwa pa munthu wolungama pamatulutsa za nzeru,
32 Milomo ya anthu olungama imadziwa zoyenera kuyankhula,