Números 28
NYA vs NTLH
1 Yehova anawuza Mose kuti,
1 O Senhor Deus disse a Moisés:
2 “Lamula Aisraeli kuti, ‘Onetsetsani kuti mukupereka kwa Ine pa nthawi yoyikika, chopereka cha chakudya chotentha pa moto monga fungo lokoma kwa Ine.’
2 — Mande que os israelitas tragam para mim, no tempo certo, as ofertas de alimento que têm um cheiro que me agrada.
3 Awuze kuti, ‘Nsembe ya chakudya imene muzipereka pa moto kwa Yehova tsiku ndi tsiku ndi iyi: Ana ankhosa a chaka chimodzi awiri, wopanda chilema.
3 — São estas as ofertas de alimento que devem ser apresentadas todos os dias e para sempre: dois carneirinhos de um ano, sem defeito.
4 Mmawa muzipereka mwana wankhosa mmodzi ndipo winayo madzulo.
4 Um deles será oferecido de manhã, e o outro, à tarde.
5 Muziperekanso kilogalamu imodzi ya ufa wosalala wosakaniza ndi lita imodzi ya mafuta a olivi.
5 Junto com cada carneirinho, será oferecido um quilo da melhor farinha de trigo misturada com um litro de azeite.
6 Iyi ndi nsembe yopsereza ya tsiku ndi tsiku imene analamula pa phiri la Sinai kuti ikhale fungo lokoma, nsembe yopsereza pa moto yopereka kwa Yehova.
6 Esse sacrifício será completamente queimado e deverá ser oferecido todos os dias. É uma oferta de alimento, de cheiro agradável a Deus, o Senhor , que foi apresentada pela primeira vez no monte Sinai.
7 Chopereka chachakumwa chikhale lita imodzi yachakumwa chaukali pa nkhosa iliyonse. Muzithira pamalo opatulika, kupereka kwa Yehova.
7 Junto com cada carneirinho, será oferecido um litro de vinho. Esse vinho deverá ser derramado no Lugar Santo , em honra do Senhor .
8 Muzipereka mwana wankhosa winayo madzulo, pamodzi ndi chopereka chachakudya monga poyamba paja ndi chopereka chachakumwa monga mmawa. Ichi ndi chopereka chachakudya, fungo lokoma kwa Yehova.’ ”
8 À tarde será oferecido o outro carneirinho, e, junto com ele, a mesma quantidade de farinha, azeite e vinho, como de manhã. Essa é uma oferta de alimento trazida para mim, o Senhor , e o seu cheiro me agrada.
9 “ ‘Pa tsiku la Sabata, muzipereka nsembe ana ankhosa awiri a chaka chimodzi wopanda chilema, pamodzi ndi chopereka chachakumwa ndi chopereka chachakudya chokwana makilogalamu awiri a ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta.
9 — No sábado serão oferecidos dois carneirinhos de um ano, sem defeito, junto com dois quilos da melhor farinha misturada com azeite, como oferta de cereais, e também uma oferta de vinho.
10 Iyi ndi nsembe yopsereza ya pa Sabata iliyonse, kuwonjezera pa nsembe yopsereza ya nthawi zonse ndi chopereka chake chachakumwa.’ ”
10 Essa oferta completamente queimada será oferecida todo sábado, além da oferta que é completamente queimada todos os dias e entregue junto com a oferta de vinho que a acompanha.
11 “Pa tsiku loyamba la mwezi uliwonse muzipereka kwa Yehova nsembe yopsereza ya ana angʼombe aamuna awiri, nkhosa yayimuna imodzi, ana ankhosa aamuna asanu ndi awiri a chaka chimodzi, onse wopanda chilema.
11 — No princípio de cada mês deem a mim, o Senhor , uma oferta que será completamente queimada. Essa oferta será de dois touros novos, um carneiro e sete carneirinhos de um ano, todos sem defeito.
12 Pa ngʼombe yayimuna iliyonse pakhale chopereka cha chakudya cha makilogalamu atatu a ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta; ndi nkhosa yayimuna, chopereka cha chakudya cha makilogalamu awiri a ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta;
12 Com cada touro novo, ofereçam três quilos da melhor farinha misturada com azeite. Com cada carneiro, ofereçam dois quilos de farinha misturada com azeite
13 ndipo pa mwana wankhosa aliyense, chopereka cha ufa wa kilogalamu imodzi ya ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta, izi ndi za nsembe yopsereza, fungo lokoma, nsembe yotentha pa moto ya kwa Yehova.
13 e, com cada carneirinho, um quilo. Essas ofertas completamente queimadas são ofertas de alimento e têm um cheiro agradável a mim, o Senhor .
14 Pa ngʼombe yayimuna iliyonse pakhale chopereka cha chakumwa cha malita awiri a vinyo; ndipo pa nkhosa yayimuna, lita limodzi ndi theka, ndipo pa mwana wankhosa, lita limodzi. Iyi ndi nsembe yopsereza ya mwezi ndi mwezi yoperekedwa pa mwezi watsopano mʼkati mwa chaka.
14 A oferta de vinho é assim: dois litros de vinho com cada touro novo, um litro e meio com cada carneiro e um litro com cada carneirinho. São essas as ofertas que serão completamente queimadas no dia primeiro de cada mês, durante o ano inteiro.
15 Powonjezera pa nsembe yopsereza ya nthawi zonse ndi chopereka chake cha chakumwa, mbuzi yayimuna imodzi iperekedwe kwa Yehova ngati nsembe yopepesera machimo.
15 Além do sacrifício que é completamente queimado e que é oferecido todos os dias e além da oferta de vinho, ofereçam também ao Senhor um bode, para tirar os pecados do povo.
16 “ ‘Pa tsiku la 14 la mwezi woyamba muzichita Paska wa Yehova.
16 — A Festa da Páscoa , comemorada em honra do Senhor Deus cai no dia catorze do primeiro mês.
17 Pa tsiku la 15 la mwezi womwewo pazikhala chikondwerero. Muzidya buledi wopanda yisiti kwa masiku asanu ndi awiri.
17 No dia quinze desse mês haverá festa. Durante sete dias vocês comerão pães feitos sem fermento.
18 Pa tsiku loyamba muzichita msonkhano wopatulika ndipo musamagwire ntchito iliyonse.
18 No primeiro dia dessa festa ninguém trabalhará; todos se reunirão para adorar a Deus.
19 Koma muzipereka kwa Yehova nsembe yotentha pa moto, nsembe yopsereza ya ana angʼombe aamuna awiri, nkhosa yayimuna imodzi ndi ana ankhosa asanu ndi awiri aamuna a chaka chimodzi, onsewo wopanda chilema.
19 Ofereçam ao Senhor um sacrifício que será completamente queimado, como oferta de alimento. Essa oferta será de dois touros novos, um carneiro e sete carneirinhos de um ano, todos sem defeito.
20 Pamodzi ndi ngʼombe yayimuna iliyonse, muzikonza chopereka cha chakudya cha makilogalamu atatu a ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta; makilogalamu awiri pa nkhosa yayimuna iliyonse.
20 Com cada touro novo, ofereçam três quilos da melhor farinha misturada com azeite. Com cada carneiro, ofereçam dois quilos de farinha misturada com azeite
21 Kilogalamu imodzi pa mwana wankhosa aliyense mwa ana ankhosa asanu ndi awiri aja.
21 e, com cada carneirinho, um quilo.
22 Muziphatikizapo mbuzi yayimuna monga nsembe yopepesera machimo anu.
22 Ofereçam também a Deus um bode como sacrifício para tirar os pecados do povo.
23 Muzikonza zimenezi nthawi zonse, powonjezera pa nsembe yopsereza ya mmawa.
23 Vocês oferecerão essas coisas, além do sacrifício que é completamente queimado todas as manhãs.
24 Motere muzikonza chakudya cha nsembe yopsereza ya tsiku ndi tsiku pa masiku asanu ndi awiri ngati fungo lokomera Yehova. Zimenezi ziziperekedwa kuwonjezera pa nsembe yopsereza ya nthawi zonse pamodzi ndi nsembe yachakumwa.
24 Assim, vocês oferecerão ao Senhor cada dia, durante sete dias, uma oferta de alimento que tem cheiro agradável a ele. Ofereçam isso, além do sacrifício que é completamente queimado todos os dias e além da oferta de vinho.
25 Pa tsiku lachisanu ndi chiwiri muzichita msonkhano wopatulika ndipo musamagwire ntchito iliyonse.
25 No sétimo dia vocês se reunirão para adorar a Deus, e ninguém trabalhará.
26 “ ‘Pa tsiku la zipatso zoyambirira kucha, pamene mukupereka chopereka cha chakudya chatsopano kwa Yehova, pa nthawi ya chikondwerero cha Masabata, muzichita msonkhano wopatulika ndipo musagwire ntchito zolemetsa.
26 — Vocês terão outra festa, chamada “ Festa da Colheita ” ou “Festa das Semanas”. No primeiro dia dessa festa, quando oferecerem a Deus, o Senhor , a nova colheita de cereais, vocês se reunirão para o adorar, e ninguém trabalhará.
27 Muzipereka nsembe zopsereza za ana angʼombe aamuna awiri, nkhosa imodzi yayimuna ndi ana ankhosa aamuna asanu ndi awiri a chaka chimodzi monga fungo lokomera Yehova.
27 Ofereçam ao Senhor um sacrifício que será completamente queimado, que tem um cheiro agradável a ele. Esse sacrifício será de dois touros novos, um carneiro e sete carneirinhos de um ano, todos sem defeito.
28 Pa ngʼombe yayimuna iliyonse pazikhala chopereka cha chakudya cha makilogalamu atatu a ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta, pa nkhosa yayimuna iliyonse makilogalamu awiri.
28 Com cada touro novo, ofereçam três quilos da melhor farinha misturada com azeite. Com cada carneiro, ofereçam dois quilos de farinha misturada com azeite
29 Ndipo pa mwana wankhosa aliyense mwa asanu ndi awiri aja, kilogalamu imodzi.
29 e, com cada carneirinho, um quilo.
30 Muziperekanso mbuzi yayimuna imodzi kuti izikhala nsembe yopepesera machimo anu.
30 Tragam também um bode como sacrifício para tirar os pecados do povo.
31 Muzipereka zimenezi pamodzi ndi zopereka za zakumwa ndi nsembe yake ya chakudya. Onetsetsani kuti nyamazo zilibe chilema.
31 Tragam isso e também a oferta de vinho, o sacrifício que é completamente queimado todos os dias e a oferta de cereais.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?