1 Yehova anawuza Yeremiya kuti,
2 “Ine Yehova, Mulungu wa Israeli ndikuti, ‘Lemba mʼbuku mawu onse amene ndakuwuza.
3 Nthawi ikubwera pamene ndidzachotse anthu anga, Israeli ndi Yuda kuchokera ku ukapolo ndi kuwabwezera dziko limene ndinapatsa makolo awo,’ akutero Yehova.”
4 Nawa mawu amene Yehova anayankhula ndi anthu a ku Israeli ndi Yuda:
5 “Yehova akuti:
6 Tsono khalani pansi ndi kudzifunsa kuti:
7 Mayo ine! Tsiku limeneli ndi lalikulu kwambiri!
8 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Pa tsiku limenelo,
9 Mʼmalo mwake, adzatumikira Yehova Mulungu wawo
10 “ ‘Tsono usachite mantha, iwe mtumiki wanga Yakobo;
11 Ine ndili nanu ndipo ndidzakupulumutsani,’
12 Yehova akuti,
13 Palibe amene angathe kukutetezani pa mlandu wanu,
14 Abwenzi anu onse akuyiwalani;
15 Chifukwa chiyani mukulira nacho chilonda chanu?
16 “Tsono onse amene anakuwonongani, nawonso adzawonongedwa;
17 Ndidzachiza matenda anu
18 Yehova akuti,
19 Anthuwo adzayimba nyimbo zoyamika Yehova
20 Ana awo adzakhalanso monga mmene analili kale,
21 Mtsogoleri wawo adzakhala mmodzi mwa iwo.
22 “Choncho inu mudzakhala anthu anga,
23 Taonani ukali wa Yehova wowomba
24 Mkwiyo woopsa wa Yehova sudzachoka