Jeremias 15

NYA

1 Kenaka Yehova anandiwuza kuti, “Ngakhale Mose ndi Samueli akanayima pamaso panga kupempherera anthu awa, Ine sindikanawachitira chisoni. Achotseni ndipo ndisawaonenso! Aleke apite!

2 Ndipo ngati akufunsa iwe kuti, ‘Kodi tipite kuti?’ uwawuze kuti, ‘Yehova akuti,

3 “Ine ndidzawatumizira mitundu inayi ya zinthu zowononga,” akutero Yehova, “lupanga lowapha, agalu owaluma, mbalame zamumlengalenga ndiponso zirombo zoti ziwadye ndi kuwawononga.

4 Ndidzawasandutsa kukhala chinthu chonyansa kwa anthu a maufumu onse a dziko lapansi chifukwa cha zimene Manase mwana wa Hezekiya mfumu ya Yuda anachita mu Yerusalemu.

5 “Kodi adzakumvera chisoni ndani, Yerusalemu?

6 Inu mwandikana Ine,” akutero Yehova.

7 Ine ndidzakubalalitsani kukuchotsani mʼmizinda ya mʼdzikomo

8 Ndinachulukitsa amayi awo amasiye

9 Mayi wa ana asanu ndi awiri wakomoka

10 Kalanga ine, amayi pakuti munandibereka ine,

11 Yehova anati,

12 “Palibe munthu amene angathe kudula chitsulo,

13 Anthu ako ndi chuma chako

14 Ndidzakusandutsani akapolo a adani anu

15 Ine ndinati, “Inu Yehova, mumadziwa zonse;

16 Munandiyankhula ndipo mawu anu ndinawalandira bwino.

17 Sindinakhale nawo mʼgulu la anthu amadyera,

18 Nanga nʼchifukwa chiyani mavuto anga sakutha?

19 Tsono Yehova anandiyankha kuti,

20 Ndidzakusandutsa ngati khoma lolimba

21 “Ndidzakupulumutsa mʼdzanja la anthu oyipa

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado