Jeremias 14

NYA

1 Awa ndi mawu amene Yehova anamuwuza Yeremiya onena za chilala:

2 “Yuda akulira,

3 Anthu awo wolemekezeka akutuma antchito awo kuti akatunge madzi.

4 Popeza pansi pawumiratu

5 Ngakhale mbawala yayikazi

6 Mbidzi zikuyima pa zitunda zopanda kanthu

7 Anthu akuti, “Ngakhale machimo athu akutitsutsa,

8 Inu Yehova amene Aisraeli amakukhulupirirani

9 Chifukwa chiyani muli ngati munthu amene wadzidzimutsidwa,

10 Zimene Yehova akunena za anthuwa ndi izi:

11 Kenaka Yehova anandiwuza kuti, “Usawapempherere anthu awa kuti zinthu ziwayendere bwino.

12 Ngakhale asale zakudya, Ine sindidzamva kulira kwawo; ngakhale apereke nsembe zopsereza ndi chopereka cha chakudya, sindidzazilandira. Mʼmalo mwake, ndidzawapha ndi lupanga, njala ndi mliri.”

13 Koma ine ndinati, “Aa, Ambuye Yehova, aneneri amawawuza anthuwo kuti, sadzaphedwa ndi lupanga kapena kuvutika ndi njala. Koma kuti Inu mudzawapatsa mtendere wokhawokha pamalo pano.”

14 Ndipo Yehova anandiwuza kuti, “Ndi zabodza kuti aneneriwa akunenera mʼdzina langa. Ine sindinawatume kapena kuwasankha kapenanso kuyankhula nawo. Iwo amakuwuzani zinthu zabodza zomwe amati anaziona mʼmasomphenya, kapena pogwiritsa ntchito mawula achabechabe. Zimene amayankhula ndi zongopeka mʼmutu mwawo.

15 Nʼchifukwa chake Ine Yehova ndikuti aneneri amenewa akulosera mʼdzina langa pamene Ine sindinawatume. Iwo amati simudzafa pa nkhondo kapena ndi njala mʼdziko muno. Koma tsono ndi iwowo, aneneriwa amene adzafe pa nkhondo kapena ndi njala.

16 Ndipo anthu amene anawaloserawo adzaponyedwa mʼmisewu ya mu Yerusalemu atafa ndi njala ndi lupanga. Sipadzapezeka wowayika mʼmanda popeza iwowo, akazi awo, ana awo aamuna, onse adzakhala atafa. Ine ndidzawagwetsera chilango chowayenera.

17 “Awuze mawu awa:

18 Ndikapita kuthengo,

19 Kodi anthu a ku Yuda mwawakana kwathunthu?

20 Inu Yehova, ife tikuvomereza kuyipa kwathu

21 Musatikane kuopa kuti dzina lanu linganyozedwe;

22 Mwa milungu yachabechabe ya anthu a mitundu ina,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado