Jeremias 10

NYA

1 Inu Aisraeli, imvani zimene Yehova akunena.

2 Yehova akuti,

3 Pakuti miyambo ya mitundu inayo ndiyachabechabe.

4 Amakongoletsa chosemacho ndi siliva ndi golide;

5 Mafano awo ali ngati mtengo wakanjedza woopsezera mbalame mʼmunda wa minkhaka.

6 Palibe wofanana nanu, Inu Yehova;

7 Ndani amene angaleke kukuopani,

8 Onsewo ndi opusa ndi opanda nzeru;

9 Siliva wosula amabwera naye kuchokera ku Tarisisi

10 Koma Yehova ndiye Mulungu woona;

11 “Awuze anthu awa kuti, ‘Milungu iyi, imene sinalenge dziko lakumwamba ndi dziko lapansi, idzawonongeka pa dziko lapansi ndi pansi pa thambo.’ ”

12 Koma Mulungu analenga dziko lapansi ndi mphamvu zake;

13 Iye akayankhula, kumamveka mkokomo wamadzi akumwamba;

14 Anthu onse ndi opusa ndiponso opanda nzeru;

15 Mafanowo ndi achabechabe, zinthu zosekedwa nazo.

16 Koma Yehova amene ndi Cholowa cha Yakobo sali ngati mafanowo.

17 Sonkhanitsani katundu wanu,

18 Pakuti Yehova akuti,

19 Aliyense ankangoti, “Mayo ine, chifukwa cha kupweteka kwanga!

20 Tenti yanga yawonongeka,

21 Abusa ndi opusa

22 Tamvani! kukubwera mphekesera,

23 Inu Yehova, ndikudziwa kuti moyo umene munthu ali nawo si wake;

24 Inu Yehova, langizeni, komatu mwachilungamo,

25 Tsanulirani ukali wanu pa mitundu ya anthu amene sakudziwani,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado