1 Ndani wakhulupirira zimene tanenazi;
2 Iye anakula ngati mphukira pamaso pake,
3 Iye ananyozedwa ndi kukanidwa ndi anthu,
4 Ndithudi, iye anamva zowawa mʼmalo mwa ife;
5 Koma iye analasidwa chifukwa cha zolakwa zathu,
6 Ife tonse, ngati nkhosa, tasochera,
7 Anthu anamuzunza ndi kumusautsa,
8 Atatha kumugwira mwankhanza ndikumuyimba mlandu, kenaka anapita naye kukamupha.
9 Anamukonzera manda ake pamodzi ndi anthu oyipa
10 Komatu ndi Yehova amene anafuna kuti amuzunze ndi kumusautsa.
11 Atatha mazunzo a moyo wake,
12 Motero Ine ndidzamupatsa ulemu pamodzi ndi akuluakulu,