1 Dzambatuka, dzambatuka iwe Ziyoni,
2 Sasa fumbi lako;
3 Pakuti Yehova akuti,
4 Pakuti Ambuye Yehova akuti,
5 Tsopano Ine Yehova ndikuti,
6 Tsono tsiku limenelo anthu anga adzadziwa dzina langa;
7 Ngokongoladi mapazi a
8 Mverani! Alonda anu akukweza mawu awo;
9 Imbani pamodzi mofuwula nyimbo zachimwemwe,
10 Yehova wagwiritsa ntchito mphamvu zake zopatulika
11 Nyamukani, nyamukani, chokaniko ku Babuloniko!
12 Koma simudzachoka mofulumira
13 Taonani, mtumiki wanga adzapambana pa ntchito yake
14 Anthu ambiri atamuona anadzidzimuka,
15 Momwemonso anthu a mitundu yonse adzadodoma naye,