Isaías 21

NYA

1 Uthenga wonena za chipululu cha mʼmbali mwa Nyanja.

2 Ine ndaona zinthu zoopsa mʼmasomphenya:

3 Chifukwa cha zimenezi thupi langa likunjenjemera ndi mantha,

4 Mtima wanga ukugunda,

5 Ankhondo a ku Elamu ndi Mediya akukonza matebulo,

6 Zimene Ambuye akunena kwa ine ndi izi;

7 Taonani, anthu akubwera ali pa akavalo

8 Ndipo mlondayo anafuwula kuti,

9 Taonani, uyo munthu akubwera atakwera pa galeta

10 Inu anthu anga opunthidwa ndi kupetedwa ngati tirigu,

11 Uthenga wonena za Duma:

12 Mlonda akuyankha kuti,

13 Uthenga wonena za Arabiya:

14 perekani madzi kwa anthu aludzu.

15 Iwo akuthawa malupanga,

16 Zimene Ambuye akunena kwa ine ndi izi: “Chaka chimodzi chisanathe, potsata mmene amawerengera munthu waganyu, ulemerero wonse wa Kedara udzatheratu.

17 Mwa anthu okoka uta, ankhondo a ku Kedara opulumuka adzakhala owerengeka.” Wayankhula ndi Yehova Mulungu wa Israeli.

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado