1 Uthenga wonena za chipululu cha mʼmbali mwa Nyanja.
2 Ine ndaona zinthu zoopsa mʼmasomphenya:
3 Chifukwa cha zimenezi thupi langa likunjenjemera ndi mantha,
4 Mtima wanga ukugunda,
5 Ankhondo a ku Elamu ndi Mediya akukonza matebulo,
6 Zimene Ambuye akunena kwa ine ndi izi;
7 Taonani, anthu akubwera ali pa akavalo
8 Ndipo mlondayo anafuwula kuti,
9 Taonani, uyo munthu akubwera atakwera pa galeta
10 Inu anthu anga opunthidwa ndi kupetedwa ngati tirigu,
11 Uthenga wonena za Duma:
12 Mlonda akuyankha kuti,
13 Uthenga wonena za Arabiya:
14 perekani madzi kwa anthu aludzu.
15 Iwo akuthawa malupanga,
16 Zimene Ambuye akunena kwa ine ndi izi: “Chaka chimodzi chisanathe, potsata mmene amawerengera munthu waganyu, ulemerero wonse wa Kedara udzatheratu.
17 Mwa anthu okoka uta, ankhondo a ku Kedara opulumuka adzakhala owerengeka.” Wayankhula ndi Yehova Mulungu wa Israeli.