Ezequiel 28

NYA

1 Yehova anandiyankhula nati:

2 “Iwe mwana wa munthu, iwuze mfumu ya ku Turo mawu a Ine Ambuye Yehova akuti,

3 Taona, ndiwedi wanzeru kupambana Danieli.

4 Mwa nzeru zako ndi kumvetsa kwako

5 Ndi nzeru zako zochitira malonda

6 “ ‘Choncho Ine Ambuye Yehova ndikuti,

7 Ine ndidzabwera ndi anthu achilendo, anthu ankhanza,

8 Iwo adzakuponyera ku dzenje

9 Kodi udzanenabe kuti, ‘Ine ndine mulungu,’

10 Udzafa imfa ya anthu osachita mdulidwe

11 Yehova anandiyankhula kuti:

12 “Iwe mwana wa munthu, imba nyimbo yodandaulira mfumu ya Turo ndipo uyiwuze mawu a Ine Ambuye Yehova akuti,

13 Iwe unkakhala ngati mu Edeni,

14 Ndinayika kerubi kuti azikulondera.

15 Makhalidwe ako anali abwino

16 Unatanganidwa ndi zamalonda.

17 Unkadzikuza mu mtima mwako

18 Ndi malonda ako achinyengo unachulukitsa machimo ako.

19 Anthu onse amitundu amene ankakudziwa

20 Yehova anandiyankhula nati:

21 “Iwe mwana wa munthu, utembenukire ku mzinda wa Sidoni ndipo unenere mowudzudzula kuti,

22 ‘Ine Ambuye Yehova ndikuti,

23 Ndidzatumiza mliri pa iwe

24 “ ‘Nthawi imeneyo Aisraeli sadzakhalanso ndi anthu pafupi achipongwe amene ali ngati nthula zowawa ndi ngati minga zopweteka. Pamenepo iwo adzadziwa kuti Ine ndine Ambuye Yehova.

25 “ ‘Ine Ambuye Yehova mawu anga ndi awa: Nditasonkhanitsa Aisraeli kuchoka ku mayiko kumene anamwazikira, ndidzadzionetsa kuti ndine woyera pakati pawo pamaso pa anthu a mitundu ina. Adzakhala mʼdziko lawo, limene ndinalipereka kwa mtumiki wanga Yakobo.

26 Adzakhala kumeneko mwamtendere ndipo adzamanga nyumba ndi kulima minda ya mpesa. Adzakhala kumeneko mwamtendere pamene ndidzalange anthu oyandikana nawo, amene ankawanyoza. Motero iwo adzadziwa kuti Ine ndine Yehova Mulungu wawo.’ ”

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado