1 Ana a Isakara anali awa:
2 Ana a Tola ndi awa:
3 Mwana wa Uzi anali
4 Monga mwa chiwerengero cha mabanja awo, panali anthu 36,000 odziwa kumenya nkhondo, pakuti iwo anali ndi akazi ndi ana ambiri.
5 Abale awo onse a mʼbanja la Isakara amene anali odziwa kumenya nkhondo analipo 87,000, olembedwa potsata mibado yawo.
6 Ana atatu a Benjamini anali awa:
7 Ana a Bela anali awa:
8 Ana a Bekeri anali awa:
9 Pa mndandanda wa mʼbado wawo panali atsogoleri a mabanja ndi anthu 20,200 odziwa kumenya nkhondo.
10 Mwana wa Yediaeli anali
11 Ana onsewa a Yediaeli anali atsogoleri a mabanja. Analipo anthu 17,200 amene anali okonzeka kupita ku nkhondo.
12 Asupi ndi Ahupi anali zidzukulu za Iri, ndipo Ahusimu anali zidzukulu za Aheri.
13 Ana a Nafutali anali awa:
14 Ana a Manase anali awa:
15 Makiri anatenga mkazi wa banja la Ahupi ndi Asupi. Mlongo wake anali Maaka.
16 Maaka mkazi wa Makiri anabereka mwana wamwamuna ndipo anamutcha Perezi. Mʼbale wake anamutcha Seresi, ndipo ana ake anali Ulamu ndi Rakemu.
17 Mwana wa Ulamu anali
18 Mlongo wake Hamoleketi anabereka Isihodi, Abiezeri ndi Mahila.
19 Ana a Semida anali:
20 Ana a Efereimu anali awa:
21 Zabadi,
22 Efereimu, abambo awo, anawalira masiku ambiri, ndipo abale ake anabwera kudzamutonthoza.
23 Kenaka anagona ndi mkazi wake, ndipo anakhala woyembekezera nabala mwana wamwamuna. Anamutcha dzina lake Beriya, chifukwa tsoka linagwera banja lake.
24 Mwana wake wamkazi anali Seera, amene anamanga mzinda wa Beti-Horoni Wakumunsi, Wakumtunda kudzanso Uzeni-Seera.
25 Mwana wina wa Efereimu anali Refa amene zidzukulu zake zinali Resefu,
26 Ladani, Amihudi,
27 Nuni
28 Malo amene ankakhala anali Beteli ndi midzi yozungulira, cha kummawa kunali Naarani, Gezeri ndi midzi yake ya kumadzulo ndi Sekemu ndi midzi yake mpaka ku Aya ndi midzi yake.
29 Mʼmbali mwa malire a Manase munali Beti-Seani, Taanaki, Megido ndi Dori, pamodzi ndi midzi yake. Zidzukulu za Yosefe mwana wa Israeli zimakhala mʼmizinda imeneyi.
30 Ana a Aseri anali awa:
31 Ana a Beriya anali awa:
32 Heberi anabereka Yafuleti, Someri, Hotamu ndi Suwa, mlongo wawo.
33 Ana a Yafuleti anali awa:
34 Ana a Someri anali awa:
35 Ana a mʼbale wake Helemu anali awa:
36 Ana a Zofa anali awa:
37 Bezeri, Hodi, Sama, Silisa, Itirani ndi Bera.
38 Ana a Yeteri anali awa:
39 Ana a Ula anali awa:
40 Onsewa anali zidzukulu za Aseri, atsogoleri a mabanja, anthu omveka, ankhondo olimba mtima, ndi akuluakulu pakati pa atsogoleri anzawo. Chiwerengero cha anthu odziwa kumenya nkhondo chomwe chinalembedwa chinali 26,000.