Salmos 71

NYA

1 Mwa Inu Yehova ine ndathawiramo;

2 Mundilanditse ndi kundipulumutsa mwa chilungamo chanu,

3 Mukhale thanthwe langa lothawirapo,

4 Landitseni Inu Mulungu wanga, kuchoka mʼdzanja la oyipa,

5 Pakuti Inu mwakhala chiyembekezo changa, Inu Ambuye Wamphamvuzonse,

6 Kuyambira pamene ndinabadwa, ndakhala ndikudalira Inu;

7 Ine ndakhala chinthu chodabwitsa kwa anthu ambiri

8 Pakamwa panga padzaza ndi matamando anu,

9 Musanditaye pamene ndakalamba;

10 Pakuti adani anga ayankhula motsutsana nane;

11 Iwo amati, “Mulungu wamusiya;

12 Musakhale kutali ndi ine Inu Mulungu,

13 Ondineneza anga awonongeke mwa manyazi,

14 Koma ine ndidzakhala ndi chiyembekezo mwa Inu nthawi zonse,

15 Pakamwa panga padzafotokoza za chilungamo chanu,

16 Ndidzabwera ndi kulengeza za machitidwe amphamvu zanu Inu Ambuye Wamphamvuzonse.

17 Kuyambira ubwana wanga, Inu Mulungu mwakhala mukundiphunzitsa,

18 Ngakhale pamene ndakalamba ndipo imvi zili mbuu

19 Mphamvu zanu ndi kulungama kwanu zimafika mpaka kumwambamwamba.

20 Ngakhale mwandionetsa mavuto

21 Inu mudzachulukitsa ulemu wanga

22 Ndidzakutamandani ndi zeze

23 Milomo yanga idzafuwula ndi chimwemwe

24 Lilime langa lidzafotokoza za ntchito zanu zachilungamo

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado