1 Inu Yehova, kumbukirani Davide
2 Iye analumbira kwa Yehova
3 “Sindidzalowa mʼnyumba mwanga
4 sindidzalola kuti maso anga agone,
5 mpaka nditamupezera malo Yehova,
6 Zoonadi, tinamva za Bokosi la Chipangano ku Efurata,
7 “Tiyeni tipite ku malo ake okhalamo;
8 ‘Dzukani Yehova, ndipo bwerani ku malo anu opumulira,
9 Ansembe anu avekedwe chilungamo;
10 Chifukwa cha Davide mtumiki wanu,
11 Yehova analumbira kwa Davide,
12 ngati ana ako azisunga pangano langa
13 Pakuti Yehova wasankha Ziyoni,
14 “Awa ndi malo anga opumapo ku nthawi za nthawi;
15 Ndidzadalitsa mzindawu ndi zinthu zambiri;
16 Ndidzaveka ansembe ake chipulumutso,
17 “Pano ndidzachulukitsa mphamvu za Davide
18 Ndidzaveka adani ake manyazi,