1 “Nena kwa abale ako kuti, ‘Ndinu anthu anga,’ kwa alongo ako kuti ‘Ndinu okondedwa anga.’ ”
2 “Dzudzulani amayi anu, adzudzuleni iwo,
3 Akapanda kutero ndidzamuvula,
4 Sindidzaonetsa chikondi changa pa ana ake,
5 Amayi awo akhala akuchita zachiwerewere
6 Choncho njira yake ndidzayitseka ndi minga;
7 Adzathamangira zibwenzi zake koma sadzazipeza;
8 Iye sanazindikire kuti ndine amene
9 “Choncho Ine ndidzamulanda tirigu wanga pa nthawi yokolola,
10 Motero tsopano ndidzaonetsa maliseche ake
11 Ndidzathetsa zikondwerero zake zonse:
12 Ndidzawononga mitengo yake ya mpesa ndi mitengo yake yamkuyu,
13 Ndidzamulanga chifukwa cha masiku
14 “Koma tsopano ndidzamukopa mkaziyo;
15 Kumeneko ndidzamubwezera minda yake ya mpesa,
16 “Tsiku limeneli,” Yehova akuti,
17 Ndidzachotsa mayina a Abaala pakamwa pake;
18 Tsiku limenelo ndidzachita pangano
19 Ndidzakutomera kuti ukhale mkazi wanga mpaka muyaya;
20 Ndidzakutomera mokhulupirika
21 “Tsiku limenelo Ine ndidzayankha,”
22 ndipo nthaka idzamvera kupempha kwa tirigu,
23 Ndidzadzala Israeli mʼdziko kuti akhale wanga: