Oséias 2

NYA

1 “Nena kwa abale ako kuti, ‘Ndinu anthu anga,’ kwa alongo ako kuti ‘Ndinu okondedwa anga.’ ”

2 “Dzudzulani amayi anu, adzudzuleni iwo,

3 Akapanda kutero ndidzamuvula,

4 Sindidzaonetsa chikondi changa pa ana ake,

5 Amayi awo akhala akuchita zachiwerewere

6 Choncho njira yake ndidzayitseka ndi minga;

7 Adzathamangira zibwenzi zake koma sadzazipeza;

8 Iye sanazindikire kuti ndine amene

9 “Choncho Ine ndidzamulanda tirigu wanga pa nthawi yokolola,

10 Motero tsopano ndidzaonetsa maliseche ake

11 Ndidzathetsa zikondwerero zake zonse:

12 Ndidzawononga mitengo yake ya mpesa ndi mitengo yake yamkuyu,

13 Ndidzamulanga chifukwa cha masiku

14 “Koma tsopano ndidzamukopa mkaziyo;

15 Kumeneko ndidzamubwezera minda yake ya mpesa,

16 “Tsiku limeneli,” Yehova akuti,

17 Ndidzachotsa mayina a Abaala pakamwa pake;

18 Tsiku limenelo ndidzachita pangano

19 Ndidzakutomera kuti ukhale mkazi wanga mpaka muyaya;

20 Ndidzakutomera mokhulupirika

21 “Tsiku limenelo Ine ndidzayankha,”

22 ndipo nthaka idzamvera kupempha kwa tirigu,

23 Ndidzadzala Israeli mʼdziko kuti akhale wanga:

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado