1 “Tsiku limenelo Debora ndi Baraki mwana wa Abinoamu anayimba nyimbo iyi:
2 “Popeza kuti atsogoleri anatsogoleradi mʼdziko la Israeli;
3 “Imvani inu mafumu! Tcherani khutu, atsogoleri inu!
4 “Inu Yehova, pamene munkatuluka mu Seiri,
5 Mapiri anagwedezeka pamaso pa Yehova,
6 “Pa nthawi ya Samugara mwana wa Anati,
7 Anthu a ku midzi anathawa; mu Israeli munalibe midzi
8 Pamene anasankha milungu ina,
9 Mtima wanga uli ndi atsogoleri a Israeli,
10 “Inu okwera pa abulu oyera,
11 Ku zitsime, kutali ndi phokoso la a mauta;
12 Anati, ‘Tsogolera ndiwe, Debora, tsogolera;
13 “Kenaka anthu okhulupirika anatsatira atsogoleri awo;
14 Anakalowa mʼchigwa kuchokera ku Efereimu;
15 Olamulira a Isakara anali pamodzi ndi Debora;
16 Chifukwa chiyani munangokhala ku makola a nkhosa nʼkumangomvetsera
17 Agiliyadi anatsala pa tsidya la Yorodani.
18 Azebuloni ndi anthu amene anayika moyo wawo mʼzoopsa.
19 “Mafumu anabwera, anachita nkhondo;
20 Ngakhalenso nyenyezi zakumwamba zinachita nkhondo,
21 Mtsinje wa Kisoni unawakokolola,
22 Ndipo ziboda za ngʼombe zazimuna zinachita phokoso lalikulu,
23 Mngelo wa Yehova anati ‘Tembererani Merozi.’
24 “Akhale wodala kupambana akazi onse,
25 Munthu uja anapempha madzi akumwa, koma iye anamupatsa mkaka;
26 Anatenga chikhomo cha tenti mʼdzanja lake,
27 Anathifukira ku mapazi a mkaziyo nagwa,
28 “Amayi ake a Sisera anasuzumira pa zenera;
29 Amayi ake anzeru kwambiri anamuyankha,
30 ‘Kodi iwo sakufunafuna zofunkha kuti agawane;
31 “Choncho Yehova! adani anu onse awonongeke,