1 Yehova anandiwuza kuti,
2 “Pita ukalengeze kwa anthu a ku Yerusalemu kuti Yehova akuti,
3 Israeli anali wopatulika wa Yehova,
4 Imvani mawu a Yehova, inu zidzukulu za Yakobo,
5 Yehova akuti,
6 Iwo sanafunse nʼkomwe kuti, ‘Kodi Yehova ali kuti,
7 Ndinakufikitsani ku dziko lachonde
8 Ansembe nawonso sanafunse kuti,
9 “Chifukwa chake Ine ndidzakuyimbaninso mlandu,”
10 Pitani kumadzulo ku chilumba cha Kitimu, ndipo mukaone,
11 Kodi ulipo mtundu wa anthu uliwonse umene unasinthapo milungu yake?
12 Inu mayiko akumwamba, dabwani ndi zimenezi,
13 “Popeza anthu anga achita machimo awiri:
14 Israeli si wantchito kapena kapolo wobadwira mʼnyumba, ayi.
15 Adani ake abangulira
16 Ndiponso Aigupto a ku Mefisi ndi a ku Tapanesi
17 Zimenezitu zakuchitikirani
18 Tsopano mudzapindula chiyani mukapita ku Igupto,
19 Kuyipa kwanuko kudzakulangani;
20 “Kuyambira kalekale inu munathyola goli lanu
21 Ine ndinakudzala iwe ngati mtengo wampesa wosankhika;
22 Ngakhale utasamba ndi soda
23 “Iwe ukunena bwanji kuti, ‘Ine sindinadziyipitse;
24 wakhala ngati mbidzi yozolowera mʼchipululu,
25 Iwe usathamange, nsapato zingakuthere kuphazi
26 “Monga momwe mbala imachitira manyazi pamene yagwidwa,
27 Iwo amawuza mtengo kuti, ‘Iwe ndiwe abambo athu,’
28 Nanga ili kuti milungu yanu imene munadzipangira nokha?
29 “Kodi mukundizengeranji mlandu?
30 “Ine ndinalanga anthu ako popanda phindu;
31 “Inu anthu a mʼbado uno, ganizirani bwino mawu a Yehova:
32 Kodi namwali amayiwala zokongoletsera zake,
33 Mumadziwa bwino njira zopezera zibwenzi!
34 Ngakhale pa zovala zako anthu amapezapo
35 inu mukunena kuti, ‘Ndife osalakwa,
36 Chifukwa chiyani
37 Mudzachokanso kumeneko