Jonas 2

NYA

1 Yona ali mʼmimba mwa chinsomba chija anapemphera kwa Yehova Mulungu wake.

2 Iye anati:

3 Munandiponya mʼnyanja yozama,

4 Ndinati, ‘Ine ndachotsedwa

5 Madzi wondimiza anandichititsa mantha,

6 Ndinatsikira kunsi ndithu, mʼtsinde mwa mapiri;

7 “Pamene moyo wanga umachoka mwa ine,

8 “Iwo amene amagwiritsitsa mafano achabechabe

9 Koma ine ndidzapereka kwa Inu nsembe

10 Ndipo Yehova analamula chinsomba chija, ndipo chinakamusanza Yonayo mʼmbali mwa nyanja.

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado