1 Yona ali mʼmimba mwa chinsomba chija anapemphera kwa Yehova Mulungu wake.
2 Iye anati:
3 Munandiponya mʼnyanja yozama,
4 Ndinati, ‘Ine ndachotsedwa
5 Madzi wondimiza anandichititsa mantha,
6 Ndinatsikira kunsi ndithu, mʼtsinde mwa mapiri;
7 “Pamene moyo wanga umachoka mwa ine,
8 “Iwo amene amagwiritsitsa mafano achabechabe
9 Koma ine ndidzapereka kwa Inu nsembe
10 Ndipo Yehova analamula chinsomba chija, ndipo chinakamusanza Yonayo mʼmbali mwa nyanja.