Ezequiel 7

NYA

1 Yehova anandipatsa uthenga uwu kuti,

2 “Iwe mwana wa munthu, Ine Ambuye Yehova ndikuwuza dziko la Israeli kuti:

3 Chimaliziro chili pa iwe tsopano.

4 Ine sindidzakumvera chisoni

5 “Zimene ndikunena Ine Ambuye Yehova ndi izi:

6 Chimaliziro chafika!

7 Inu anthu okhala mʼdziko,

8 Ine ndili pafupi kukukwiyirani,

9 Ine sindidzakumvera chisoni

10 “Taona, tsikulo!

11 Chiwawa chasanduka ndodo

12 Nthawi yafika!

13 Wogulitsa sadzazipezanso zinthu

14 “Lipenga lalira,

15 Ku bwalo kuli kumenyana

16 Onse amene adzapulumuka

17 Dzanja lililonse lidzalefuka,

18 Iwo adzavala ziguduli

19 “Iwo adzataya siliva wawo mʼmisewu

20 Iwo ankanyadira zodzikongoletsera zawo zamakaka

21 Ndidzazipereka kwa alendo kuti azifunkhe.

22 Ine ndidzawalekerera anthuwo

23 “Konzani maunyolo,

24 Ndidzabweretsa mitundu ya anthu oyipitsitsa

25 Nkhawa ikadzawafikira

26 Tsoka lidzatsatana ndi tsoka linzake,

27 Mfumu idzalira,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado