1 Yehova anandipatsa uthenga uwu kuti,
2 “Iwe mwana wa munthu, Ine Ambuye Yehova ndikuwuza dziko la Israeli kuti:
3 Chimaliziro chili pa iwe tsopano.
4 Ine sindidzakumvera chisoni
5 “Zimene ndikunena Ine Ambuye Yehova ndi izi:
6 Chimaliziro chafika!
7 Inu anthu okhala mʼdziko,
8 Ine ndili pafupi kukukwiyirani,
9 Ine sindidzakumvera chisoni
10 “Taona, tsikulo!
11 Chiwawa chasanduka ndodo
12 Nthawi yafika!
13 Wogulitsa sadzazipezanso zinthu
14 “Lipenga lalira,
15 Ku bwalo kuli kumenyana
16 Onse amene adzapulumuka
17 Dzanja lililonse lidzalefuka,
18 Iwo adzavala ziguduli
19 “Iwo adzataya siliva wawo mʼmisewu
20 Iwo ankanyadira zodzikongoletsera zawo zamakaka
21 Ndidzazipereka kwa alendo kuti azifunkhe.
22 Ine ndidzawalekerera anthuwo
23 “Konzani maunyolo,
24 Ndidzabweretsa mitundu ya anthu oyipitsitsa
25 Nkhawa ikadzawafikira
26 Tsoka lidzatsatana ndi tsoka linzake,
27 Mfumu idzalira,