1 “Imba nyimbo ya madandawulo, kuyimbira akalonga a ku Israeli.
2 Uzinena kuti,
3 Unalera mmodzi mwa ana ake,
4 Anthu amitundu anamva za mkangowo,
5 “ ‘Amayi aja ataona kuti mwana ankamukhulupirira uja wagwidwa ndi kuti chiyembekezo chake chapita padera,
6 Unkayendayenda pakati pa mikango inzake,
7 Unagwetsa malinga awo,
8 Pamenepo mitundu ya anthu, makamaka ochokera madera ozungulira,
9 Anawukoka ndi ngowe nawuponya mʼchitatanga.
10 “ ‘Amayi ako anali ngati mpesa mʼmunda wamphesa
11 Nthambi zake zinali zolimba,
12 Koma unazulidwa mwaukali
13 Ndipo tsopano anawuwokeranso ku chipululu,
14 Moto unatulukanso mu mtengomo