Eclesiastes 7

NYA

1 Mbiri yabwino ndi yopambana mafuta onunkhira bwino,

2 Kuli bwino kupita ku nyumba yamaliro

3 Chisoni nʼchabwino kusiyana ndi kuseka,

4 Mtima wa munthu wanzeru nthawi zonse umalingalira za imfa,

5 Kuli bwino kumva kudzudzula kwa munthu wanzeru

6 Kuseka kwa zitsiru kuli ngati

7 Kuzunza ena kumasandutsa munthu wanzeru kukhala chitsiru,

8 Mathero ake a chinthu ndi abwino kupambana chiyambi chake,

9 Usamafulumire kukwiya mu mtima mwako,

10 Usamafunse kuti, “Nʼchifukwa chiyani masiku amakedzana anali abwino kupambana masiku ano?”

11 Nzeru ngati cholowa, ndi chinthu chabwino

12 Nzeru ndi chitetezo,

13 Taganizirani zimene Mulungu wazichita:

14 Pamene zinthu zili bwino, sangalala;

15 Pa moyo wanga wopanda phinduwu ndaona zinthu ziwiri izi:

16 Usakhale wolungama kwambiri

17 Usakhale woyipa kwambiri,

18 Nʼkwabwino kuti utsate njira imodzi,

19 Nzeru zimapereka mphamvu zambiri kwa munthu wanzeru

20 Palibe munthu wolungama pa dziko lapansi

21 Usamamvetsere mawu onse amene anthu amayankhula,

22 pakuti iwe ukudziwa mu mtima mwako

23 Zonsezi ndinaziyesa ndi nzeru zanga ndipo ndinati,

24 Nzeru zimene zilipo,

25 Kotero ndinayikapo mtima wanga kuti ndidziwe,

26 Ndinapeza kanthu kowawa kupambana imfa,

27 Mlaliki akunena kuti, “Taonani, chimene ndinachipeza ndi ichi:

28 pamene ine ndinali kufufuzabe

29 Chokhacho chimene ndinachipeza ndi ichi:

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado