2 Samuel 22

NYA

1 Davide anayimbira Yehova nyimbo iyi pamene Yehovayo anamupulumutsa mʼdzanja la adani ake onse ndiponso mʼdzanja la Sauli.

2 Iye anati,

3 Mulungu wanga ndiye thanthwe langa, mʼmene ndimathawiramo,

4 “Ndimayitana Yehova amene ndi woyenera matamando,

5 “Mafunde a imfa anandizinga;

6 Anandimanga ndi zingwe za ku manda;

7 “Mʼmasautso anga ndinapemphera kwa Yehova;

8 “Dziko lapansi linanjenjemera ndi kuchita chivomerezi,

9 Mʼmphuno mwake munatuluka utsi;

10 Iye anangʼamba thambo natsika pansi;

11 Iye anakwera pa Kerubi ndi kuwuluka;

12 Iye anapanga mdima kukhala chofunda chake,

13 Mʼkuwala kumene kunali pamaso pake

14 Yehova anabangula kumwamba ngati bingu,

15 Iye anaponya mivi yake, nabalalitsa adani ake,

16 Zigwa za mʼnyanja zinaonekera poyera,

17 “Ali kumwamba, Iye anatambalitsa dzanja lake ndipo anandigwira;

18 Anandipulumutsa kwa mdani wanga wamphamvu,

19 Adaniwo analimbana nane pamene ndinali pa mavuto,

20 Iye anandipititsa kumalo otakasuka;

21 “Yehova wandithandiza molingana ndi chilungamo changa;

22 Pakuti ine ndinatsata njira za Yehova;

23 Malamulo ake onse ali pamaso panga,

24 Ndakhala moyo wosalakwa pamaso pake

25 Yehova wandipatsa mphotho molingana ndi chilungamo changa,

26 “Kwa wokhulupirika, Inu mumaonetsa kukhulupirika kwanu,

27 Kwa woyera mtima, Inu mumaonetsa kuyera mtima kwanu,

28 Inu mumapulumutsa anthu odzichepetsa,

29 Inu Yehova, ndinu nyale yanga;

30 Ndi thandizo lanu nditha kulimbana ndi gulu la ankhondo,

31 “Kunena za Mulungu, zochita zake ndi zangwiro;

32 Mulungu wina ndi uti wofanana nanu Yehova?

33 Ndi Mulungu amene anandipatsa mphamvu

34 Iye amasandutsa mapazi anga kukhala ngati ambawala yayikazi;

35 Iye amaphunzitsa manja anga kuchita nkhondo;

36 Inu mundipatsa ine chishango chanu cha chigonjetso;

37 Inu mwalimbitsa njira yanga kuti ndiyende bwino,

38 “Ine ndinathamangitsa adani anga ndi kuwakantha;

39 Ndinawakantha kotheratu, ndipo sanathe kudzukanso;

40 Inu munandipatsa ine mphamvu yochitira nkhondo;

41 Inu muchititsa kuti adani anga atembenuke ndi kuthawa;

42 Iwo anafuwula kupempha thandizo, koma panalibe ndi mmodzi yemwe owapulumutsa.

43 Ine ndinawaperesa ngati fumbi la pa dziko lapansi;

44 “Inu mwandipulumutsa mʼmanja mwa mitundu ya anthu;

45 Alendo amadzipereka okha pamaso panga;

46 Iwo onse anataya mtima;

47 “Yehova ndi wamoyo! Litamandidwe Thanthwe langa.

48 Iye ndi Mulungu amene amabwezera chilango,

49 amene amandimasula mʼmanja mwa adani anga.

50 Choncho ine ndidzakutamandani Inu Yehova, pakati pa anthu a mitundu ina;

51 “Iye amapereka chipambano chachikulu kwa mfumu yake,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado